Thokozani Mnolo

Thokozani Mnolo

Ndizotheka Kuteteza Chilengedwe Ndi Zinyalala

Potsatira maphunziro, omwe anali nawo mwezi wa May okhudza kapangidwe kamakala ochokera kuzinyalala, achinyamata a gulu la Kafoteka mu boma la Mzimba ayamba kupanga paokha makalawa. Guliri, lomwe limachokera m’mudzi mwa Inkosi Mmbelwa, lati atachita maphunziro wa kwatsiku limodzi anaona…

Youthful Social Worker Empowers Community

Timothy Mwale, a 23-year-old social worker and communications specialist, has taken an initiative to empower vulnerable children and youths in his community through education and social initiatives. Mwale’s journey to becoming a dedicated social worker and founder of Orphans of…

Achinyamata Aku Mzimba Ayamba Kuteteza Chilengedwe

M’modzi mwa achinyamata omwe akugwira ntchito yofuna kuteteza chilengedwe m’boma la Mzimba Anthony Botha wayamba ntchito yophunzitsa achinyamata kapangidwe kamakala otchedwa ‘briquettes’ m’chingereezi. Botha yemwe akugwira ntchitoyi mongodzipereka wati anachiona chanzeru kuphunzitsa achinyamatawa potengera kuti achinyamata ali ndi udindo waukulu…